Versuri
intro
Dark. venom. venom. ifendamalawiiii. intro gaye!!!!
chorus
tsiku lina ndidzamwalila anthu ena adzandilila lekelenji kusangalala pamene ine ndili moyo
tsikuli ndidzamwalila anthu ena adzandifochela lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyo
ndikapeza ndalama ndimweko fanta ndikapeza ndalama ndidyeko soseji pamene ine ndili moyo.
verse
ndimweko malawi jini. kuchekuche konyagi wavutayiii ndalama zikatha ndilolela eee kupinyolitsa tayiii ndagulitsa fodya nandolo soya mtedza ndine bambo apemphelo kwathu mkumayaniii. kudedza. lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyooooo
chorus
tsiku lina ndidzamwalila anthu ena adzandilila lekelenji kusangalala pamene ine ndili moyo
tsikuli ndidzamwalila anthu ena adzandifochela lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyo
ndikapeza ndalama ndimweko fanta ndikapeza ndalama ndidyeko soseji pamene ine ndili moyo.
verse2
ikenga the pango. wachiyawo wangalusa. ndilekelenji. kumwako mowa. chosecho moyowu. ndiwaufupi. tandilekeni ndinjoyeletu. poti. kumanda. kulibe. matsuna. gwileko ka jeni. tionge. ndi. magi. mwina. moyowu. mkuwupepesa nde ndilekelenji kusangalala. pamene ine. ndilimoyooo
chorus
tsiku lina ndidzamwalila anthu ena adzandilila lekelenji kusangalala pamene ine ndili moyo
tsikuli ndidzamwalila anthu ena adzandifochela lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyo
ndikapeza ndalama ndimweko fanta ndikapeza ndalama ndidyeko soseji pamene ine ndili moyo
Dark. venom. venom. ifendamalawiiii. intro gaye!!!!
chorus
tsiku lina ndidzamwalila anthu ena adzandilila lekelenji kusangalala pamene ine ndili moyo
tsikuli ndidzamwalila anthu ena adzandifochela lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyo
ndikapeza ndalama ndimweko fanta ndikapeza ndalama ndidyeko soseji pamene ine ndili moyo.
verse
ndimweko malawi jini. kuchekuche konyagi wavutayiii ndalama zikatha ndilolela eee kupinyolitsa tayiii ndagulitsa fodya nandolo soya mtedza ndine bambo apemphelo kwathu mkumayaniii. kudedza. lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyooooo
chorus
tsiku lina ndidzamwalila anthu ena adzandilila lekelenji kusangalala pamene ine ndili moyo
tsikuli ndidzamwalila anthu ena adzandifochela lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyo
ndikapeza ndalama ndimweko fanta ndikapeza ndalama ndidyeko soseji pamene ine ndili moyo.
verse2
ikenga the pango. wachiyawo wangalusa. ndilekelenji. kumwako mowa. chosecho moyowu. ndiwaufupi. tandilekeni ndinjoyeletu. poti. kumanda. kulibe. matsuna. gwileko ka jeni. tionge. ndi. magi. mwina. moyowu. mkuwupepesa nde ndilekelenji kusangalala. pamene ine. ndilimoyooo
chorus
tsiku lina ndidzamwalila anthu ena adzandilila lekelenji kusangalala pamene ine ndili moyo
tsikuli ndidzamwalila anthu ena adzandifochela lekelenji kusangalala pamene ine ndilimoyo
ndikapeza ndalama ndimweko fanta ndikapeza ndalama ndidyeko soseji pamene ine ndili moyo